Ndikayang'ana kutali
Mtima wanga umazama
Ndimalota za tsiku lina
Nditafika kwathuko
Kopanda misozi
Kopanda ululu
Yahuah adzandilandila
Mu dziko la lonjezolo
Chorus
Tidzakhala mu mtendele (Shalom)
Tidzakhala ndi chimwemwe (shalom)
Tidzadya zipatso zabwino
Tidzamwa mu mitsinje
Tidzayimba mosatopa (HaleluYah)
Tidzaseka limodzi tonse (HaleluYah)
Yahuah adzakhala nafe
Mu dziko la lonjezolo
Verse 2
Minda yobiliwira
Mitengo idzabala
Mitsinjenso yodzaza
Madzi oyela bwino
Ana adzathamanga
Akulu adzaseka
Sipadzakhala kulila
Mu dziko la lonjezolo
Chorus
Tidzakhala mu mtendele (Shalom)
Tidzakhala ndi chimwemwe (shalom)
Tidzadya zipatso zabwino
Tidzamwa mu mitsinje
Tidzayimba mosatopa (HaleluYah)
Tidzaseka limodzi tonse (HaleluYah)
Yahuah adzakhala nafe
Mu dziko la lonjezolo
Bridge
Pamene tili tikuyenda
Tiyembekeza tsikulo
Chiyembekezo sidzatha
Yahuah sasinthanso
Tiyeni tilimbike
Tisabwelele m'mbuyo
Posachedwa tidzafika
Mu dziko la lonjezolo
Final Chorus
Tidzakhala mu mtendele (Shalom)
Tidzakhala ndi chimwemwe (shalom)
Tidzadya zipatso zabwino
Tidzamwa mu mitsinje
Tidzayimba mosatopa (HaleluYah)
Tidzaseka limodzi tonse (HaleluYah)
Yahuah adzakhala nafe
Mu dziko la lonjezolo
Estilo de Música
1980 country gospel duet
Editar título de la canción
Información de licencia
Editar portada de la cancion
Haz clic abajo para subir una portada cuadrada
Tamano recomendado: 360x360 o superior (proporcion 1:1)